Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 June tsamba 7
  • “Umutulire Yehova Nkhawa Zako”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Umutulire Yehova Nkhawa Zako”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Senzani Yehova Nkhaŵa Yanu Nthaŵi Zonse
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Zimene Zingatithandize Tikakhala ndi Nkhawa
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • “Mulungu Ndiye Mthandizi Wanga”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Umutulire Yehova Nkhawa Zako
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 June tsamba 7

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 52-59

“Umutulire Yehova Nkhawa Zako”

Davide anakumana ndi mayesero ambiri othetsa nzeru. Pamene Salimo 55 linkalembedwa, n’kuti atakumana ndi zinthu monga . . .

  • Goliati ndi mtumiki wake

    Kunyozedwa

  • Davide akuzinda muvi

    Kuzunzidwa

  • Davide akuvutika maganizo chifukwa chodziimba mlandu

    Kudziimba Mlandu

  • Batiseba akulira

    Mavuto a M’banja

  • Davide akudwala ndipo ali pabedi

    Kudwala

  • Davide waukiridwa

    Kuukiridwa

Davide anakwanitsa kupirira mavuto ake ngakhale kuti mavutowo ankaoneka ngati amukulira. Iye analemba malangizo othandiza anthu omwe amaona kuti n’zovuta kupirira mayesero omwe akukumana nawo. Anati: “Umutulire Yehova nkhawa zako.”

Kodi tingagwiritse ntchito bwanji vesili masiku ano?

55:22

Davide akupemphera
  1. Tizipemphera kwa Yehova mochokera pansi pamtima tikakumana ndi vuto linalake komanso ngati tikuda nkhawa ndi zinazake

  2. Tizifufuza malangizo opezeka m’Mawu a Yehova komanso omwe gulu lake limapereka

  3. Tiziyesetsa kupeza mfundo za m’Baibulo zomwe zingatithandize kuchepetsa mavuto omwe takumana nawo

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena