Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 June tsamba 6
  • “Mulungu Ndiye Mthandizi Wanga”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Mulungu Ndiye Mthandizi Wanga”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • “Umutulire Yehova Nkhawa Zako”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Yehova Amathandiza Anthu Amene Amamudalira
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2004
  • Mulungu Azikutsogolerani M’zinthu Zonse
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Anthu Amene Amakhulupirira Yehova Amakhala Olimba Mtima
    Nsanja ya Olonda—2011
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 June tsamba 6

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

“Mulungu Ndiye Mthandizi Wanga”

Masalimo 52–59 amasonyeza mmene Davide ankamvera pa nthawi yomwe ankakumana ndi mavuto. Komabe anakhulupirira Yehova pa nthawi yovutayi. (Sal. 54:4; 55:22) Iye anatamandanso Yehova chifukwa cha Mawu ake. (Sal. 56:10) Kodi ifeyo timakhulupirira komanso kudalira Mulungu ngati mmene Davide ankachitira? Kodi tikakumana ndi mavuto, timafufuza malangizo m’Mawu a Yehova? (Miy. 2:6) Kodi ndi mavesi ati omwe anakuthandizani pamene . . .

  • munafooka kapena kuvutika maganizo?

  • munkadwala?

  • ena anakukhumudwitsani?

  • munkazunzidwa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena