Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 September tsamba 2
  • September 5-11

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 5-11
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 September tsamba 2

September 5-11

SALIMO 119

  • Nyimbo Na. 48 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “‘Muzitsatira Chilamulo cha Yehova’”: (10 min.)

    • Sal. 119:1-8—Kutsatira chilamulo cha Mulungu n’kumene kumatichititsa kukhalabe osangalala (w05 4/15 10 ndime 3-4)

    • Sal. 119:33-40—Mawu a Mulungu amatithandiza kuti tikhale olimba mtima tikamakumana ndi mavuto (w05 4/15 13 ndime 12)

    • Sal. 119:41-48—Kudziwa bwino Mawu a Mulungu kumatithandiza kuti tizilalikira molimba mtima (w05 4/15 13 ndime 13-14)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Sal. 119:71—Kodi kukumana ndi mavuto kuli ndi ubwino wotani? (w06 9/1 14 ndime 4)

    • Sal. 119:96—Kodi mawu akuti “zinthu zonse zabwino kwambiri zili ndi malire” akutanthauza chiyani? (w06 9/1 14 ndime 5)

    • Kodi ndaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Sal. 119:73-93

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Kukonzekera Ulaliki wa Mwezi Uno: (15 min.) Nkhani yokambirana. Pambuyo poonetsa vidiyo ya chitsanzo cha ulaliki iliyonse, kambiranani mfundo zikuluzikulu za m’vidiyoyi. Limbikitsani ofalitsa kuti alembe ulaliki wawowawo.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 69

  • “Kodi Tingatani Ngati Tapeza Mwana Pakhomo Lomwe Tikufuna Kulalikira?”: (5 min.) Nkhani.

  • Zofunika Pampingo: (10 min.) Ngati palibe, mukhodza kukambirana zimene tikuphunzira mu Buku Lapachaka (yb16 59-62)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 6 ndime 1-14.

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 13 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena