Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 June tsamba 2
  • June 5-11

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • June 5-11
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 June tsamba 2

June 5-11

YEREMIYA 51-52

  • Nyimbo Na. 37 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Nthawi Zonse Mawu a Yehova Amakwaniritsidwa”: (10 min.)

    • Yer. 51:11, 28​—Yehova ananeneratu za munthu amene adzagonjetse Babulo (it-2-E 360 ¶2-3)

    • Yer. 51:30​—Yehova ananeneratu kuti Babulo adzawonongedwa (it-2-E 459 ¶4)

    • Yer. 51:37, 62​—Yehova ananeneratu kuti Babulo adzakhala bwinja (it-1-E 237 ¶1)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Yer. 51:25​—Kodi n’chifukwa chiyani Babulo akutchulidwa kuti ndi “phiri lowononga”? (it-2-E 444 ¶9)

    • Yer. 51:42​—Kodi “nyanja” imene ‘idzasefukire ndi kumiza Babulo,’ ikuimira chiyani? (it-2-E 882 ¶3)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yer. 51:1-11

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Kukonzekera Ulaliki wa Mwezi Uno: (15 min.) Kukambirana “Zitsanzo za Ulaliki.” Pambuyo poonetsa vidiyo ya chitsanzo cha ulaliki iliyonse, kambiranani mfundo zikuluzikulu za m’vidiyoyo. Limbikitsani ofalitsa kuti azionetsa mwininyumba zimene zili pa webusaiti yathu ya jw.org/ny pa gawo lakuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > MFUNDO ZOTHANDIZA MABANJA.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 152

  • “Kodi Mumakhulupirira Kwambiri Zimene Yehova Analonjeza”: (15 min.) Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Limbikitsani onse kuti nthawi zonse azikambirana maulosi a m’Baibulo ndi Akhristu anzawo n’cholinga choti azilimbitsa chikhulupiriro chawo.​—Aroma 1:11, 12.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 2 ¶1-12

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 49 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena