Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 June tsamba 6
  • June 26–July 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • June 26–July 2
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 June tsamba 6

June 26–July 2

Ezekieli 6-10

  • Nyimbo Na. 141 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kodi Mudzalembedwa Chizindikiro Choti Ndinu Woyenera Kupulumuka?”: (10 min.)

    • Ezek. 9:1, 2​—Masomphenya amene Ezekieli anaona ndi othandizanso kwa ife (w16.06 16-17)

    • Ezek. 9:3, 4​—Pa nthawi ya chisautso chachikulu, anthu amene amamvetsera tikamawalalikira adzalembedwa chizindikiro choti ndi oyenera kupulumuka

    • Ezek. 9:5-7​—Yehova sadzawononga anthu olungama pamodzi ndi oipa

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Ezek. 7:19​—Kodi vesi limeneli lingatithandize bwanji kukonzekera zam’tsogolo? (w09 9/15 23 ¶10)

    • Ezek. 8:12​—Kodi vesili likusonyeza bwanji kuti munthu amene alibe chikhulupiriro n’zosavuta kuti achite zoipa? (w11 4/15 26 ¶14)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ezek. 8:1-12

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Chiv. 4:11​—Kuphunzitsa Choonadi.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Sal. 11:5; 2 Akor. 7:1​—Kuphunzitsa Choonadi.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bh 127 ¶4-5​—Sonyezani mmene tingafikire pamtima wophunzira wathu.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 64

  • “Tizitsatira Mfundo za Makhalidwe Abwino za Yehova”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo yakuti Khalani Bwenzi La Yehova​—Mwamuna Mmodzi, Mkazi Mmodzi (imapezeka pamene palembedwa kuti ANA).

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 2 ¶35-40, komanso tsamba 25, 26-27, 28-29

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 33 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena