Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 July tsamba 6
  • July 24-30

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 24-30
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 July tsamba 6

July 24-30

EZEKIELI 21-23

  • Nyimbo Na. 99 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Ufumu Unaperekedwa kwa Amene Ndi Woyenerera Mwalamulo”: (10 min.)

    • Ezek. 21:25​—“Mtsogoleri wa Isiraeli woipa” anali Mfumu Zedekiya (w07 7/1 13 ¶11)

    • Ezek. 21:26​—Anthu a m’banja la Davide omwe ankalamulira ali ku Yerusalemu anasiya kukhala mafumu (w11 8/15 9 ¶6)

    • Ezek. 21:27​—Yesu Khristu ndi amene ali “woyenerera mwalamulo” kukhala Mfumu (w14 10/15 10 ¶14)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Ezek. 21:3​—Kodi “lupanga” limene Yehova anasolola m’chimake ndi chiyani makamaka? (w07 7/1 14 ¶1)

    • Ezek. 23:49​—Kodi chaputala 23 chikusonyeza kuti Aisiraeli ndi Ayuda anachita tchimo lotani, nanga ifeyo tikuphunzirapo chiyani? (w07 7/1 14 ¶6)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ezek. 21:1-13

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) fg​—Mufotokozereni za vidiyo yakuti Kodi Phunziro la Baibulo Limachitika Bwanji? (Koma musaonetse vidiyoyi).

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) bhs​—Mufotokozereni munthu amene mumam’patsa magazini mwezi uliwonse za vidiyo yakuti Kodi Phunziro la Baibulo Limachitika Bwanji? (Koma musaonetse vidiyoyi).

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bhs 217 ¶1-3

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 93

  • “Tizisonyeza Ulemu Tikafika Pakhomo”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Ikambidwe ndi woyang’anira utumiki. Yambani ndi kuonetsa vidiyo yofotokoza zimene tingachite kuti tizisonyeza ulemu tikafika pakhomo la munthu.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 4 ¶7-15 komanso tsamba 44, 46

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 29 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena