Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 July tsamba 6
  • Ufumu Unaperekedwa kwa Amene Ndi Woyenerera Mwalamulo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ufumu Unaperekedwa kwa Amene Ndi Woyenerera Mwalamulo
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • “Kuteteza . . . ndi Kukhazikitsa Mwalamulo Ntchito ya Uthenga Wabwino”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Mmene Yehova Amatithandizira Kukwaniritsa Utumiki Wathu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Ezekieli Anasangalala Kulengeza Uthenga wa Mulungu
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Ezekieli—Gawo 1
    Nsanja ya Olonda—2007
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 July tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EZEKIELI 21-23

Ufumu Unaperekedwa kwa Amene Ndi Woyenerera Mwalamulo

Losindikizidwa

Pokwaniritsa ulosi wa Ezekieli, Yesu ndi amene anali “woyenerera mwalamulo” kukhala mfumu.

  • Yuda

    Gen. 49:10

    Kodi Mesiya anabadwira mu mtundu uti?

  • Davide

    2 Sam. 7:12, 16

    Kodi ndi ufumu uti umene Yehova ananena kuti udzakhazikika mpaka kalekale

  • Yosefe

    Mat. 1:16

    Kodi Mateyu anati Yesu anali wa mu mzera wobadwira chifukwa cha kholo liti?

Yesu

Kodi tikuphunzirapo chiyani za Yehova pa zomwe anachita posankha Yesu kukhala mfumu yoikidwa mwalamulo?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena