Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 July tsamba 7
  • July 31–August 6

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 31–August 6
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 July tsamba 7

July 31–August 6

EZEKIELI 24-27

  • Nyimbo Na. 81 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Ulosi Wonena za Kuwonongedwa kwa Turo Umatithandiza Kuti Tizikhulupirira Kwambiri Mawu a Yehova”: (10 min.)

    • Ezek. 26:3, 4​—Kutatsala zaka zoposa 250, Yehova ananeneratu kuti mzinda wa Turo udzawonongedwa (si 133 ¶4)

    • Ezek. 26:7-11​—Ezekieli anatchula mfumu komanso mtundu wa anthu womwe udzayambirire kuukira mzinda wa Turo (ce 216 ¶3)

    • Ezek. 26:4, 12​—Ezekieli ananeneratu kuti mpanda, fumbi komanso nyumba za mumzinda wa Turo zidzaponyedwa m’madzi (it-1 70)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Ezek. 24:6, 12​—Kodi dzimbiri la mphika likuimira chiyani? (w07 7/1 14 ¶2)

    • Ezek. 24:16, 17​—N’chifukwa chiyani Ezekieli sankafunika kusonyeza chisoni pamene mkazi wake anamwalira? (w88 9/15 21 ¶24)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ezek. 25:1-11

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Kapepala kalikonse​—Muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Kapepala kalikonse​—Mufotokozereni za vidiyo yakuti Kodi Phunziro la Baibulo Limachitika Bwanji? (Koma musaonetse vidiyoyi).

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bhs 23 ¶13-15​—Muitanireni kumisonkhano.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 134

  • Kukhulupirira Mawu a Mulungu Kumatithandiza Kupirira Tikakumana ndi Mayesero: (15 min.) Nkhani yokambirana yochokera pa malemba monga Yesaya 33:24; 65:21, 22; Yohane 5:28, 29 ndi Chivumbulutso 21:4. Onetsani vidiyo yakuti Kuyamikira Madalitso Amene Ufumu Udzabweretse. Limbikitsani onse kuti azidziyerekezera ali m’dziko latsopano, makamaka pamene akumana ndi mayesero.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 4 ¶16-23, komanso tsamba 48

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 88 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena