Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 August tsamba 4
  • August 14-20

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • August 14-20
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 August tsamba 4

August 14-20

EZEKIELI 32-34

  • Nyimbo Na. 144 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Udindo Waukulu wa Mlonda”: (10 min.)

    • Ezek. 33:7​—Yehova anaika Ezekieli kukhala mlonda (it-2 1172 ¶2)

    • Ezek. 33:8, 9​—Mlonda akachenjeza anthu ankapewa mlandu wamagazi (w88 1/1 28 ¶13)

    • Ezek. 33:11, 14-16​—Yehova adzapulumutsa anthu amene amamvera akachenjezedwa (w12 3/15 15 ¶3)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Ezek. 33:32, 33​—N’chifukwa chiyani tiyenera kupitirizabe kulalikira ngakhale kuti anthu ena amatitsutsa kapena kutinyoza? (w91 3/15 17 ¶16-17)

    • Ezek. 34:23​—Kodi vesi limeneli likukwaniritsidwa bwanji? (w07 4/1 26 ¶3)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ezek. 32:1-16

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) g17.4 chikuto​—Muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) g17.4 chikuto​—Muitanireni kumisonkhano.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg phunziro 2 ¶9-10​—Sonyezani mmene tingafikire pamtima wophunzira wathu.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 67

  • “Muzikhala ndi Makhalidwe Amene Mulungu Amasangalala Nawo​—Kulimba Mtima”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo yakuti Muzipewa Zinthu Zimene Zingawononge Khalidwe Lanu la Kukhulupirika​—Kuopa Anthu.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 5 ¶10-17 komanso tsamba 53

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 117 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena