Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 October tsamba 4
  • October 9-15

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • October 9-15
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 October tsamba 4

October 9-15

DANIELI 10-12

  • Nyimbo Na. 31 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yehova Ananeneratu Zokhudza Mafumu a Mtsogolo”: (10 min.)

    • Dan. 11:2​—Mafumu 4 analamulira mu ufumu wa Perisiya (dp 212-213 ¶5-6)

    • Dan. 11:3​—Alekizanda Wamkulu anaonekera (dp 213 ¶8)

    • Dan. 11:4​—Ufumu wa Alekizanda unagawanika n’kukhala maufumu 4 (dp 214 ¶11)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Dan. 12:3​—Kodi “anthu ozindikira” ndi ndani, nanga ndi liti pamene “adzawala ngati kuwala kwa kuthambo”? (w13 7/15 13 ¶16, mawu akumapeto)

    • Dan. 12:13​—Kodi Yehova anamulonjeza chiyani Danieli? (dp 315 ¶18)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Dan. 11:28-39

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) g17.5 chikuto​—Muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) g17.5 chikuto​—Pitirizani kukambirana zokhudza magazini imene munamupatsa kale. Muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Nkhani: (Osapitirira 6 min.) w16.11 5-6 ¶7-8​—Mutu: Kodi Tingatsanzire Bwanji Chitsanzo cha Yehova pa Nkhani Yolimbikitsa Ena?

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 113

  • Timalimbikitsidwa ndi Maulosi a M’Baibulo: (15 min.) Onetsani vidiyo yakuti ‘Mawu a Ulosi’ Amatilimbikitsa.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 8 ¶8-13, komanso tsamba 83

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 126 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena