Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 March tsamba 5
  • Mapeto a Dziko Loipali Ali Pafupi Kwambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mapeto a Dziko Loipali Ali Pafupi Kwambiri
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—1997
  • Nthaŵi ya Kudikira
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Kodi Kukhalapo kwa Khristu Kumatanthauza Chiyani kwa Inu?
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Opulumuka ku “Mbadwo Woipa”
    Nsanja ya Olonda—1995
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 March tsamba 5
Yesu akuyankhula ndi Petulo, Andireya, Yakobo ndi Yohane

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Mapeto a Dziko Loipali Ali Pafupi Kwambiri

Onerani vidiyo yakuti, Mapeto a Dziko Loipali Ali Pafupi Kwambiri, ndipo kenako kambiranani mafunso otsatirawa omwe ndi okhudza lemba la Mateyu 24:34.

Tchati chofotokoza za “m’badwo uwu”
  • Kodi “zinthu zonsezi” zomwe zatchulidwa palembali ndi chiyani?

  • Kodi lemba la Ekisodo 1:6 limatithandiza bwanji kumvetsa tanthauzo la mawu akuti “m’badwo”?

  • Kodi Yesu ankanena za m’badwo uti kwenikweni?

  • Kodi ndi magulu awiri ati amene apanga “m’badwo uwu”?

  • Kodi mawu a Yesu akusonyeza bwanji kuti tikukhala m’nthawi yamapeto yeniyeni?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena