Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 October tsamba 8
  • Akhristu Oona Amadziwika Chifukwa cha Chikondi​—Muzisangalala ndi Choonadi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Akhristu Oona Amadziwika Chifukwa cha Chikondi​—Muzisangalala ndi Choonadi
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • “Chikondi . . . Sichikondwera ndi Zosalungama”
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Kondwerani mwa Yehova!
    Nsanja ya Olonda—1994
  • Tiyeni Tisangalale Limodzi
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Anthu a Yehova Amakana Kuchita Zosalungama
    Nsanja ya Olonda—2014
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 October tsamba 8

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Akhristu Oona Amadziwika Chifukwa cha Chikondi​—Muzisangalala ndi Choonadi

KODI ZIMENEZI N’ZOFUNIKA BWANJI? Potengera chitsanzo cha Yesu, tiyenera kumayesetsa kuchitira umboni choonadi chokhudza zolinga za Mulungu. (Yoh. 18:37) Tiyeneranso kumasangalala ndi choonadi, kulankhula zoona komanso kupitirizabe kuganizira zinthu zilizonse zoona ngakhale kuti tikukhala m’dziko limene anthu ambiri ndi achinyengo komanso opanda chilungamo.​—1 Akor. 13:6; Afil. 4:8.

KODI TINGACHITE BWANJI ZIMENEZI?

  • Tisamamvetsere kapena kufalitsa nkhani zamiseche.​—1 Ates. 4:11

  • Tisamasangalale anthu ena akakumana ndi mavuto

  • Tizisangalala ndi zinthu zabwino komanso zolimbikitsa

ONERANI VIDIYO YAKUTI ‘MUZIKONDANA’​—MUZISANGALALA NDI CHOONADI, OSATI NDI ZOSALUNGAMA, KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Kodi Debbie anasonyeza bwanji kuti ‘ankasangalala ndi zosalungama’?

  • Kodi Alice anasintha bwanji nkhani imene Debbie ankakamba n’kuyamba kukambirana zolimbikitsa?

  • Kodi ndi zinthu zina ziti zolimbikitsa zimene tingakambirane?

Alice akulankhulana ndi Debbie

Muzisangalala ndi choonadi, osati ndi zosalungama

CHITSANZO CHA M’BAIBULO CHOFUNIKA KUCHIGANIZIRA: Loti ankavutika chifukwa cha makhalidwe oipa a anthu a ku Sodomu ndi Gomora.​—2 Pet. 2:8.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndingasonyeze bwanji kuti ndimasangalala ndi choonadi, osati ndi zosalungama?’

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena