Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 January tsamba 6
  • January 28–February 3

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • January 28–February 3
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 January tsamba 6

January 28–February 3

MACHITIDWE 27-28

  • Nyimbo Na. 129 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Paulo Anapita ku Roma”: (10 min.)

    • Mac. 27:23, 24​—Mngelo anauza Paulo kuti iyeyo ndi onse omwe anali m’ngalawamo apulumuka mphepo yamkuntho (bt 208 ¶15)

    • Mac. 28:1, 2​—Ngalawa imene Paulo anakwera inasweka pachilumba cha Melita (bt 209 ¶18-210, ¶21)

    • Mac. 28:16, 17​—Paulo anakafika bwinobwino ku Roma (bt 213 ¶10)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Mac. 27:9​—Kodi “nthawi ya kusala kudya kwa Tsiku la Mwambo Wophimba Machimo” imatanthauza chiyani? (“kusala kudya kwa Tsiku la Mwambo Wophimba Machimo” mfundo zimene ndikuphunzira pa Mac. 27:9, nwtsty)

    • Mac. 28:11​—Kodi chochititsa chidwi n’chiyani ndi kutchulidwa kwa chizindikiro chomwe chinali pangalawa yomwe Paulo anakwera? (“Ana . . . a Zeu” mfundo zimene ndikuphunzira pa Mac. 28:11, nwtsty)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mac. 27:1-12 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza wachiwiri. (th phunziro 2)

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 5 min.) lv 139-140 ¶16-17 (th phunziro 3)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 103

  • “Paulo Anayamika Mulungu Ndipo Analimba Mtima”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani mbali ina ya vidiyo yakuti “Chitsulo Chimanola Chitsulo Chinzake.” Limbikitsani onse kuti akaonere vidiyo yonse kunyumba kwawo.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 23 ndi bokosi lakuti “Munthu Wogwidwa ndi Mzimu Woipa”

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 140 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena