Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 May tsamba 3
  • May 13-19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • May 13-19
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 May tsamba 3

May 13-19

2 Akorinto 7-10

  • Nyimbo Na. 109 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Utumiki Wothandiza Anthu pa Nthawi ya Mavuto”: (10 min.)

    • 2 Akor. 8:1-3​—Akhristu a ku Makedoniya anachita “zoposa” zimene akanatha pothandiza abale awo a ku Yudeya (w98 11/1 25 ¶1; kr 209 ¶1)

    • 2 Akor. 8:4​—Tikamathandiza Akhristu omwe akuvutika timakhala tikuchita “utumiki wothandiza” anthu (kr 209-210 ¶4-6)

    • 2 Akor. 9:7​—“Mulungu amakonda munthu wopereka mokondwera” (kr 196 ¶10)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • 2 Akor. 9:15​—Kodi ‘mphatso ya Mulungu yaulere imene sitingathe kuifotokoza’ n’chiyani? (w16.01 12 ¶2)

    • 2 Akor. 10:17​—Kodi ‘kudzitamanda mwa Yehova’ kumatanthauza chiyani? (g99 7/8 27)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) 2 Akor. 7:1-12 (th phunziro 12)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. (th phunziro 1)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire pa nkhani inayake yomwe anthu a m’gawo lanu amatsutsa kawirikawiri. (th phunziro 2)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire pa nkhani inayake yomwe anthu a m’gawo lanu amatsutsa kawirikawiri. (th phunziro 4)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 17

  • “Mmene Utumiki Wothandiza Anthu pa Nthawi ya Mavuto Wathandizira Akhristu a ku Caribbean”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Chikondi Chimaonekera ndi Zochita​—Ntchito Yothandiza Anthu pa Zilumba za Caribbean.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 35 ¶28-36

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 89 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena