Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 June tsamba 6
  • “Musamade Nkhawa ndi Kanthu Kalikonse”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Musamade Nkhawa ndi Kanthu Kalikonse”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • N’chiyani Chingandithandize Ndikakhala Ndi Nkhawa?
    Zimene Achinyamata Amafunsa
  • Muzimutulira Yehova Nkhawa Zanu Zonse
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • ‘Mtendere wa Mulungu Umaposa Kuganiza Mozama Kulikonse’
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Tayani Nkhaŵa Yanu Yonse pa Yehova
    Nsanja ya Olonda—1994
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 June tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AFILIPI 1-4

“Musamade Nkhawa ndi Kanthu Kalikonse”

4:6, 7

Mlongo akupemphera, kenako akumva bwino mumtima
  • Pemphero lingatithandize kuti tisamakhale ndi nkhawa

  • Tikamapemphera tili ndi chikhulupiriro, Yehova amatipatsa mtendere womwe “umaposa kuganiza mozama kulikonse”

  • Ngakhale zitakhala kuti palibe zimene tingachite ndi vuto lathulo, Yehova angatithandize kuti tipirire. Angathenso kutithandiza m’njira imene sitimaiganizira.​—1 Akor. 10:13

Kodi ndi zinthu ziti zomwe zimandidetsa nkhawa?

Kodi ndingasonyeze bwanji kuti ndimadalira kwambiri Yehova?

Mlongo akuda nkhawa chifukwa cha ngongole; mlongo wachikulire akupemphera atakhala pambali pa bedi la mwamuna wake yemwe akudwala; makolo akukangana ana awo akuona
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena