Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 July tsamba 5
  • July 22-28

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 22-28
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 July tsamba 5

July 22-28

1 TIMOTEYO 1-3

  • Nyimbo Na. 103 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yesetsani Kuti Mukhale Oyang’anira”: (10 min.)

    • [Onerani vidiyo yakuti Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la 1 Timoteyo.]

    • 1 Tim. 3:1​—Abale onse akulimbikitsidwa kuti aziyesetsa kuti akhale oyang’anira mumpingo (w16.08 21 ¶3)

    • 1 Tim. 3:13​—Abale amene amatumikira bwino amalandira madalitso ambiri (km 9/78 4 ¶7)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • 1 Tim. 1:4​—N’chifukwa chiyani Paulo anachenjeza Timoteyo kuti asamataye nthawi kukambirana ndi anthu nkhani zokhudza mibadwo ya makolo? (it-1 914-915)

    • 1 Tim. 1:17​—N’chifukwa chiyani Yehova yekha ndi amene ayenera kutchedwa “Mfumu yamuyaya”? (cl 12 ¶15)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) 1 Tim. 2:1-15 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza wachiwiri. (th phunziro 2)

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 5 min.) lvs 47-48 ¶6-7 (th phunziro 6)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 137

  • Achinyamata Analemekeza Yehova ku Warwick: (6 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako kambiranani mafunso otsatirawa:

    Kodi abale ndi alongo achinyamata anathandiza bwanji ntchito yomanga ku Warwick, nanga anapindula bwanji?

    Kodi abale ndi alongo achinyamata angalemekeze bwanji Yehova mumpingo?

  • “Mungaphunzire Zambiri Kuchokera kwa Achikulire”: (9 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti, Muzilemekeza Abale Achikulire.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 43 ndime 19-29

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 67 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena