Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 July tsamba 6
  • July 29–August 4

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 29–August 4
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 July tsamba 6

July 29–August 4

1 TIMOTEYO 4-6

  • Nyimbo Na. 80 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kukhala Wodzipereka kwa Mulungu N’kofunika Kuposa Chuma”: (10 min.)

    • 1 Tim. 6:6-8​—Kufunika kokhala “wodzipereka kwa Mulungu ndi kukhala wokhutira ndi zimene tili nazo” (w03 6/1 9 ¶1-2)

    • 1 Tim. 6:9​—Mavuto amene anthu ofunitsitsa kulemera amakumana nawo (g 6/07 6 ¶2)

    • 1 Tim. 6:10​—Mavuto omwe amabwera chifukwa chokonda ndalama (g 11/08 6 ¶4-6)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • 1 Tim. 4:2​—Kodi munthu amaononga bwanji chikumbumtima chake, ndipo zimenezi ndi zoopsa bwanji? (lvs 23-24 ¶17)

    • 1 Tim. 4:13​—N’chifukwa chiyani Paulo analimbikitsa Timoteyo kuti azikhala wodzipereka pa nkhani yowerenga pamaso pa anthu? (it-2 714 ¶1-2)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) 1 Tim. 4:1-16 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza wachiwiri. Muitanireni kumisonkhano yathu. (th phunziro 11)

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 4 min.) lvs 207-209 ¶20-21 (th phunziro 3)

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 5 min.) Sonyezani zimene mungachite mukamasiya kuphunzira Baibulo ndi munthu amene sakupita patsogolo.​—Onani mwb19.02 7. (th phunziro 12)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 37

  • Kukonda Chuma N’koopsa: (7 min.) Onerani vidiyo yakuti, Tiyenera ‘Kuthamanga Mopirira’​—Tizipewa Zinthu Zosafunika Zomwe Zingangotitopetsa, kenako kambiranani zimene tikuphunzira.

  • “Kudzipereka kwa Mulungu N’kofunika Kuposa Kuchita Masewera”: (8 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti, Zimene Muyenera Kudziwa pa Nkhani Yochita Masewera.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 44

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 59 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena