Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 October tsamba 4
  • October 21-27

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • October 21-27
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 October tsamba 4

October 21-27

1 PETULO 3-5

  • Nyimbo Na. 14 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Mapeto a Zinthu Zonse Ayandikira”: (10 min.)

    • 1 Pet. 4:7—“Khalani oganiza bwino, ndipo khalani maso kuti musanyalanyaze kupemphera” (w13 11/15 3 ¶1)

    • 1 Pet. 4:8—“Khalani okondana kwambiri” (w99 4/15 22 ¶3)

    • 1 Pet. 4:9—“Muzicherezana popanda kudandaula” (w18.03 14-15 ¶2-3)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • 1 Pet. 3:19, 20—Kodi ndi liti pamene Yesu “anapita kukalalikira kwa mizimu imene inali m’ndende” nanga anachita bwanji zimenezi? (w13 6/15 23)

    • 1 Pet. 4:6—Kodi “uthenga wabwino unalengezedwa” kwa “akufa” ati? (w08 11/15 21 ¶8)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) 1 Pet. 3:8-22 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Woyamba: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. (th phunziro 6)

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 5 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. Yerekezerani kumuonetsa vidiyo yakuti, N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuphunzira Baibulo? kenako kambiranani naye mfundo za m’vidiyoyi. (th phunziro 8)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 137

  • “Munthu Akhoza Kusintha Akaona Ulemu Komanso Khalidwe Lanu Labwino”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Yehova Amatilimbikitsa Kuti Tithe Kulimbana ndi Mavuto Athu.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 56

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 36 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena