Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsamba 2
  • May 4-10

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • May 4-10
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 May tsamba 2

MAY 4-10

GENESIS 36-37

  • Nyimbo Na. 114 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yosefe Anachitiridwa Nsanje”: (10 min.)

    • Gen. 37:3, 4​—Azichimwene ake a Yosefe anayamba kudana naye chifukwa choti bambo ake ankamukonda kwambiri (w14 8/1 12-13)

    • Gen. 37:5-9, 11​—Maloto omwe Yosefe analota anachititsa kuti azichimwene ake azimuchitira nsanje kwambiri (w14 8/1 13 ¶2-4)

    • Gen. 37:23, 24, 28​—Yosefe anachitiridwa zankhanza ndi azichimwene ake chifukwa cha nsanje

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Gen. 36:1​—N’chifukwa chiyani Esau anapatsidwanso dzina lakuti Edomu? (it-1 678)

    • Gen. 37:29-32​—N’chifukwa chiyani azichimwene ake a Yosefe anakaonetsa Yakobo mkanjo wa Yosefe uli ndi magazi? (it-1 561-562)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Gen. 36:1-19 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Kulankhula Zomveka, kenako kambiranani phunziro 17 m’kabuku ka Kuphunzitsa.

  • Nkhani: (Osapitirira 5 min.) w02 10/15 30-31​—Mutu: N’chifukwa Chiyani Akhristu Ayenera Kukhala ndi Nsanje Yofanana ndi ya Mulungu? (th phunziro 6)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 126

  • “Kodi Mwakonzekera?”: (15 min.) Nkhani yokambirana yokambidwa ndi mkulu. Onerani vidiyo yakuti Zimene Tingachite Pokonzekera Masoka Achilengedwe. Tchulaninso zilengezo zochokera ku ofesi ya nthambi kapena ku bungwe la akulu ngati zilipo.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 83

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 108 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena