Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 August tsamba 4
  • August 10-16

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • August 10-16
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 August tsamba 4

August 10-16

EKISODO 15-16

  • Nyimbo Na. 149 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Tamandani Yehova Poimba Nyimbo”: (10 min.)

    • Eks 15:1, 2​—Mose ndi amuna a Chiisiraeli anaimba nyimbo zotamanda Yehova (w95 10/15 11 ¶11)

    • Eks 15:11, 18​—Yehova ndi woyenera kutamandidwa (w95 10/15 11-12 ¶15-16)

    • Eks 15:20, 21​—Miriamu ndi akazi a Chiisiraeli anaimba nyimbo zotamanda Yehova (it-2 454 ¶1; 698)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Eks 16:13​—Pamene Aisiraeli anali m’chipululu, kodi n’kutheka kuti Yehova anasankha kuwapatsa zinziri pa zifukwa ziti? (w11 9/1 14)

    • Eks 16:32-34​—Kodi mtsuko wa mana unkasungidwa kuti? (w06 1/15 31)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Eks 16:1-18 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi ndipo kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Kodi a Linda anagwiritsa ntchito bwanji mafunso mwaluso? Kodi anafotokoza bwanji Malemba momveka bwino?

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako mugawireni buku kapena kabuku kopezeka pa Zinthu Zophunzitsira. (th phunziro 3)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 5 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako musonyezeni ndi kukambirana naye mfundo za m’vidiyo yakuti Kodi Phunziro la Baibulo Limachitika Bwanji? (koma musaonetse vidiyoyi). (th phunziro 9)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 81

  • “Muzitamanda Yehova Pochita Upainiya”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Alongo Atatu Apachibale a ku Mongolia. Kenako funsani m’bale kapena mlongo amene akutumikira monga mpainiya kapena amene anatumikirapo m’mbuyomu mafunso otsatirawa: Kodi mwakumanapo ndi mavuto otani? Ndi madalitso ati amene mwapeza?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 95

  • Mawu Omaliza (Osapitirira 3 min.)

  • Nyimbo Na. 131 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena