Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsamba 5
  • November 20-26

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • November 20-26
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 November tsamba 5

November 20-26

YOBU 18-19

  • Nyimbo Na. 44 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Musamasiye Akhristu Anzanu”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Yob 19:​1, 2—Kodi tikuphunzira chiyani pa mmene Yobu anayankhira anzake omwe anamulankhula mawu opweteka? (w94 10/1 32)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Yobu 18:​1-21 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (3 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire munthu amene wanena zinthu zomwe anthu amakonda kunena ngati sakufuna kuti tikambirane nawo. (th phunziro 12)

  • Ulendo Wobwereza: (4 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo wobwereza. Muitanireni kumisonkhano yathu ndipo yerekezerani kumuonetsa vidiyo yakuti Kodi pa Nyumba ya Ufumu Pamachitika Zotani?, kenako kambiranani naye mfundo za muvidiyoyi. (th phunziro 3)

  • Nkhani: (5 min.) w20.10 17 ¶10-11—Mutu: Muzilimbikitsa Ophunzira Baibulo Kuti Apeze Anzawo Mumpingo. (th phunziro 20)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 90

  • Khalani Bwenzi la Yehova—Uzithandiza Ena: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako ngati n’zotheka funsani ana omwe munawasankhiratu mafunso awa: Kodi ana angathandize bwanji anthu ena?

    Kodi ungakonde kuchita chiyani kuti uthandize ena?

  • “Kulimbikitsa Anthu Omwe Amatumikira pa Beteli”: (10 min.) Nkhani yokambirana komanso vidiyo.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) bt mutu 2 ¶8-15

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 63 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena