Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb24 March tsamba 13
  • April 22-28

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • April 22-28
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2024
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2024
mwb24 March tsamba 13

APRIL 22-28

MASALIMO 32-33

Nyimbo Na. 103 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. N’chifukwa Chiyani Muyenera Kuulula Tchimo Lalikulu?

(10 min.)

Davide ankavutika mumtima mwake pamene ankabisa tchimo lake, mwina lomwe anachita ndi Batiseba (Sl 32:3, 4; w93 3/15 9 ¶7)

Davide anaulula tchimolo kwa Yehova ndipo anamukhululukira (Sl 32:5; cl 262 ¶8)

Davide anamva bwino Yehova atam’khululukira (Sl 32:1; w01 6/1 29 ¶7)

Zithunzi: 1. M’bale wachinyamata akudzimvera chisoni ndipo wagwira kunkhope kwake. 2. Akupemphera. 3. Wakumana ndi akulu awiri. 4. Tsopano akumwetulira chifukwa ali ndi chikumbumtima choyera.

Tikachita tchimo lalikulu tiyenera kuvomereza modzichepetsa n’kuulula zomwe tachitazo kwa Yehova ndiponso kumupempha kuti atikhululukire. Tiyeneranso kupempha thandizo kwa akulu, omwe angatithandize kukhalanso pa ubwenzi wabwino ndi Yehova. (Yak 5:14-16) Tikachita zimenezi Yehova amatitsitsimula.​—Mac 3:19.

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Sl 33:6​—Kodi “mpweya” wa m’kamwa mwa Yehova n’chiyani? (w06 5/15 19 ¶13)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Sl 33:1-22 (th phunziro 11)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Kudzichepetsa​—Zomwe Paulo Anachita

(7 min.) Nkhani yokambirana. Onerani VIDIYO, kenako kambiranani kabuku ka lmd phunziro 4 mfundo 1-2.

5. Kudzichepetsa​—Zomwe Mungachite Potsanzira Paulo

(8 min.) Nkhani yokambirana kuchokera mu kabuku ka lmd phunziro 4 mfundo 3-5 ndi “Onaninso Malemba Awa.”

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 74

6. Zofunika Pampingo

(15 min.)

7. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 8 ¶22-24, bokosi patsamba 67

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 39 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena