Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb24 July tsamba 12
  • August 12-18

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • August 12-18
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2024
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2024
mwb24 July tsamba 12

AUGUST 12-18

MASALIMO 73-74

Nyimbo Na. 36 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Kodi Ndimachitira Nsanje Anthu Amene Satumikira Mulungu?

(10 min.)

Tikhoza kuyamba kuchitira nsanje anthu amene satumikira Yehova (Sl 73:3-5; w20.12 19 ¶14)

Tikamalambira Yehova limodzi ndi abale ndi alongo athu m’malo modzipatula, tikhoza kuyamba kuwaona bwino anthu amene satumikira Mulungu (Sl 73:17; Miy 18:1; w20.12 19 ¶15-16)

Anthu omwe satumikira Mulungu ali “pamalo oterera”; pomwe amene amamutumikira amawapatsa “ulemerero” (Sl 73:18, 19, 24; w14 4/15 4 ¶5; w13 2/15 25-26 ¶3-5)

Mtsikana wa Mboni akuyang’ana mwansanje anzake a kusukulu amene akucheza mosangalala uku akuyang’ana pafoni.

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Sl 74:13, 14—Kodi mawu akuti “Leviyatani” amanena za chiyani? (it-2 240)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Sl 74:1-23 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(3 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Pezani mwayi woti muuze mnzanu zimene mwaphunzira pa misonkhano yampingo yaposachedwapa. (lmd phunziro 2 mfundo 4)

5. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KULALIKIRA M’MALO OPEZEKA ANTHU AMBIRI. M’pempheni kuti muziphunzira naye Baibulo ndipo musonyezeni mmene phunziro limachitikira. (lmd phunziro 8 mfundo 3)

6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupirira

(5 min.) Nkhani. ijwbq 89​—Mutu: Kodi Zipembedzo Zonse N’zabwino? (th phunziro 14)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 72

7. Zofunika Pampingo

(15 min.)

8. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 14 ¶1-6, bokosi patsamba 112

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 98 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena