Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • ijwbq nkhani 15
  • Kodi Yesu Ndi Mulungu Wamphamvuyonse?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Yesu Ndi Mulungu Wamphamvuyonse?
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Yankho la m’Baibulo
  • Yesu Kristu—Mwana Wokondedwa wa Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1988
  • Kodi Yesu ndi Mulungu Wamphamvuyonse?
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Kodi Malemba Amanenanji za “Umulungu wa Kristu”?
    Nsanja ya Olonda—1992
  • Kudziwa Zoona Zokhudza Atate, Mwana, ndi Mzimu Woyera
    Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni?
Onani Zambiri
Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
ijwbq nkhani 15
Yesu

Kodi Yesu Ndi Mulungu Wamphamvuyonse?

Yankho la m’Baibulo

Anthu amene ankatsutsa Yesu anamunamizira kuti iye ananena zoti ndi wofanana ndi Mulungu. (Yohane 5:18; 10:30-33) Komabe, Yesu sananene kuti iye anali wofanana ndi Mulungu Wamphamvuyonse. Iye anati: “Atate ndi wamkulu kuposa ine.”—Yohane 14:28.

Anthu oyambirira amene ankatsatira Yesu sankamuona kuti anali wofanana ndi Mulungu Wamphamvuyonse. Mwachitsanzo, mtumwi Paulo analemba kuti Yesu ataukitsidwa, Mulungu “anamukweza n’kumuika pamalo apamwamba.” Apa zikuonekeratu kuti Paulo sankakhulupirira zoti Yesu anali Mulungu Wamphamvuyonse. Zikanakhala kuti Yesu ndi Mulungu Wamphamvuyonse, kodi zikanatheka bwanji kuti akwezedwe n’kukhala pamalo apamwamba?—Afilipi 2:9.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena