Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • nwt tsamba 480
  • Zimene Zili Mʼbuku la Rute

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Zili Mʼbuku la Rute
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Nkhani Yofanana
  • Anali “Mkazi Wabwino Kwambiri”
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
  • Ukwati Wosayembekezeka wa Boazi ndi Rute
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Anali “Mkazi Wabwino Kwambiri”
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Rute
    Nsanja ya Olonda—2005
Onani Zambiri
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Zimene Zili Mʼbuku la Rute

RUTE

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Banja la Elimeleki linasamukira ku Mowabu (1, 2)

    • Naomi, Olipa ndi Rute anakhala amasiye (3-6)

    • Rute anakhala wokhulupirika kwa Naomi ndi Mulungu wake (7-17)

    • Naomi anabwerera ku Betelehemu ndi Rute (18-22)

  • 2

    • Rute anakakunkha mʼmunda wa Boazi (1-3)

    • Rute anakumana ndi Boazi (4-16)

    • Rute anauza Naomi kuti Boazi anamukomera mtima (17-23)

  • 3

    • Naomi anapereka malangizo kwa Rute (1-4)

    • Rute ndi Boazi kopunthira mbewu (5-15)

    • Rute anabwerera kwa Naomi (16-18)

  • 4

    • Boazi anakhala wowombola (1-12)

    • Boazi ndi Rute anabereka Obedi (13-17)

    • Mzere wa makolo a Davide (18-22)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena