Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • nwt tsamba 816
  • Zimene Zili Mʼbuku la Nehemiya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Zili Mʼbuku la Nehemiya
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Nkhani Yofanana
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Nehemiya
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Mpanda wa Yerusalemu Unamangidwanso
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • “Pitirizani Kugonjetsa Choipa mwa Kuchita Chabwino”
    Nsanja ya Olonda—2007
  • “Inu Mulungu Wanga, Mundikumbukire pa Zabwino Zimene Ndinachita”
    Nsanja ya Olonda—2011
Onani Zambiri
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Zimene Zili Mʼbuku la Nehemiya

NEHEMIYA

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Uthenga wochokera ku Yerusalemu (1-3)

    • Pemphero la Nehemiya (4-11)

  • 2

    • Nehemiya anatumizidwa ku Yerusalemu (1-10)

    • Nehemiya anayendera mpanda (11-20)

  • 3

    • Ntchito yokonza mpanda (1-32)

  • 4

    • Ntchito inkayenda bwino ngakhale kuti ankatsutsidwa (1-14)

    • Anthu ankamanga atanyamula zida (15-23)

  • 5

    • Nehemiya analetsa kudyerana masuku pamutu (1-13)

    • Nehemiya sanali wodzikonda (14-19)

  • 6

    • Anthu ankatsutsabe ntchito yomanga (1-14)

    • Mpanda unamalizidwa mʼmasiku 52 (15-19)

  • 7

    • Mageti a mzinda ndiponso alonda apageti (1-4)

    • Anthu amene anabwera ku ukapolo (5-69)

      • Atumiki apakachisi (46-56)

      • Ana a atumiki a Solomo (57-60)

    • Zopereka zothandiza pa ntchito (70-73)

  • 8

    • Anawerengera anthu Chilamulo ndiponso kuwafotokozera (1-12)

    • Anachita Chikondwerero cha Misasa (13-18)

  • 9

    • Anthu analapa machimo awo (1-38)

      • Yehova ndi Mulungu wokhululuka (17)

  • 10

    • Anthu anavomereza kuti azitsatira Chilamulo (1-39)

      • “Sitidzanyalanyaza nyumba ya Mulungu wathu” (39)

  • 11

    • Anthu anayambiranso kukhala ku Yerusalemu (1-36)

  • 12

    • Ansembe ndiponso Alevi (1-26)

    • Mwambo wotsegulira mpanda (27-43)

    • Kuthandiza ntchito zapakachisi (44-47)

  • 13

    • Zinthu zinanso zimene Nehemiya anasintha (1-31)

      • Kupereka chakhumi (10-13)

      • Osaipitsa tsiku la Sabata (15-22)

      • Anawaletsa kukwatirana ndi anthu a mitundu ina (23-28)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena