Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • nwt tsamba 1570
  • Zimene Zili M‘buku la Yoweli

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Zili M‘buku la Yoweli
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Nkhani Yofanana
  • Itanirani pa Dzina la Yehova ndi Kupulumuka!
    Nsanja ya Olonda—1989
  • Kodi ‘Adzapulumuka Ndani’?
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Apereka Chiweruzo m’Chigwa Chotsirizira Mlandu
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Musachoke ‘M’chigwa cha Pakati pa Mapiri’
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Onani Zambiri
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Zimene Zili M‘buku la Yoweli

YOWELI

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Mliri woopsa wa ziwala ndi dzombe (1-14)

    • “Tsiku la Yehova lili pafupi” (15-20)

      • Mneneri anaitana Yehova (19, 20)

  • 2

    • Tsiku la Yehova komanso gulu lalikulu la asilikali ake (1-11)

    • Anawauza kuti abwerere kwa Yehova (12-17)

      • “Ngʼambani mitima yanu” (13)

    • Yehova anayankha anthu ake (18-32)

      • “Ndidzapereka mzimu wanga”  (28)

      • Zodabwitsa kumwamba ndi padziko lapansi (30)

      • Oitana pa dzina la Yehova adzapulumuka (32)

  • 3

    • Yehova adzaweruza mitundu yonse ya anthu (1-17)

      • Chigwa cha Yehosafati (2, 12)

      • Chigwa choweruzira (14)

      • Yehova, malo othawirako a Isiraeli (16)

    • Yehova adzadalitsa anthu ake (18-21)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena