Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 December tsamba 4
  • Musachoke ‘M’chigwa cha Pakati pa Mapiri’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Musachoke ‘M’chigwa cha Pakati pa Mapiri’
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Khalanibe Otetezeka M’chigwa cha Yehova
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Zamoyo za ku Chigwa Chotchedwa Death Valley
    Galamukani!—2006
  • Chigwa cha Ela—Kumene Davide Anaphera Chimphona!
    Nsanja ya Olonda​—1990
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 December tsamba 4
Anthu akuyenda ‘m’chigwa cha pakati pa mapiri’

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | ZEKARIYA 9-14

Musachoke ‘M’chigwa cha Pakati pa Mapiri’

14:3-5

Yehova anapanga “chigwa chachikulu kwambiri” mu 1914 pamene anakhazikitsa Ufumu wa Mesiya, womwe uli ngati “phiri” locheperapo poyerekezera ndi ulamuliro wake wachilengedwe chonse. Kuyambira mu 1919, atumiki a Mulungu akhala ali wotetezeka ‘m’chigwa cha pakati pa mapiri’ chimenechi.

Kodi anthu amathawira bwanji “kuchigwa” cha chitetezo?

14:12, 15

Aliyense amene ali kunja kwa chigwa chophiphiritsachi adzawonongedwa pa nkhondo ya Aramagedo

Kodi ndingatani kuti ndikhalebe m’chigwa cha chitetezo

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena