Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g02 7/8 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2002
  • Nkhani Yofanana
  • Kutetezedwa Ndi Apolisi N’kolimbitsa Mtima Komanso N’kokayikitsa
    Galamukani!—2002
  • Kodi Apolisi Ndi Ofunika Chifukwa Chiyani?
    Galamukani!—2002
  • Kodi Apolisi Ali ndi Tsogolo Lotani?
    Galamukani!—2002
  • Kodi Ndingapewe Bwanji Kuona Zithunzi Zolaula?
    Galamukani!—2007
Onani Zambiri
Galamukani!—2002
g02 7/8 tsamba 1-2

Zamkatimu

July 8, 2002

Kodi Apolisi Timawafuna Chifukwa Chiyani?

Padziko lonse, apolisi amalimbana ndi chintchito choonetsetsa kuti anthu akutsatira malamulo a boma ndiponso kuti akukhala mwabata. Kodi zinthu zikuwayendera bwanji?

3 Kodi Apolisi Ndi Ofunika Chifukwa Chiyani?

5 Kutetezedwa Ndi Apolisi N’kolimbitsa Mtima Komanso N’kokayikitsa

10 Kodi Apolisi Ali ndi Tsogolo Lotani?

16 Achinyamata Akufunsa Kuti . . .

Kodi Mnzanga Amene Ndimagona Naye M’chipinda Chimodzi Ndingagwirizane Naye Bwanji?

19 Ukapolo Ndi Khalidwe Lankhanza Lomwe Lidakalipobe

20 Tinayamba Kalekale Kulimbana Ndi Ukapolo

22 Nthaŵi Imene Ukapolo Udzathe!

27 Ndinali Wandale Tsopano Ndinasanduka Mkristu Wosakhudzidwa N’zandale

32 “Kanafika pa Nthaŵi Yofunika”

Kodi Kutengeka ndi Zithunzi Zolaula Kulibe Vuto Lililonse? 13

Kodi ndi mfundo za m’Baibulo zotani zimene zimagwira ntchito pa nkhani yokhudza zithunzi zolaula? Kodi zithunzi zimenezi zimangowasangalatsa anthu popanda kuwasokoneza m’njira inayake? Kapena kodi zingathedi kum’sokoneza Mkristu kuti asamachite zinthu zoyenera?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena