Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g02 9/8 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2002
  • Nkhani Yofanana
  • Mphaka Amene Ali Pangozi Kwambiri Padziko Lonse Lapansi
    Galamukani!—2004
  • Mfundo Zodalirika Zokhudza Tsogolo Lathu
    Galamukani!—2002
  • Anthu Amatengeka Mtima Ndi Manambala
    Galamukani!—2002
  • Kodi Muyenera Kudalira Manambala Pazochita Zanu?
    Galamukani!—2002
Onani Zambiri
Galamukani!—2002
g02 9/8 tsamba 1-2

Zamkatimu

September 8, 2002

Zinyalala—Kodi Tichita Kukwiririka Nazo?

Anthu akuchita zinthu zochulukitsa zinyalala kuposa kale lonse, ndipo zimenezi zikupangitsa kuti chilengedwe chikhale ndi mavuto osaneneka. Kodi ndi zinthu zotani zimene zachititsa kuti anthu akhale owononga chonchi, ndipo kodi tingalimbane nazo bwanji?

3 Kukhala M’dziko Lokonda Kutaya Zinthu

5 Kodi Pali Njira Yothetsera Vutoli?

9 Kulimbana Ndi Mavuto a M’dziko Lokonda Kutaya Zinthu

15 Kugwiritsa Ntchito Galamukani! Mwanjira Yabwino

19 Manambala—Kodi Mumakhudzidwa Nawo?

20 Anthu Amatengeka Mtima Ndi Manambala

22 Kodi Muyenera Kudalira Manambala Pazochita Zanu?

25 Mfundo Zodalirika Zokhudza Tsogolo Lathu

26 Mapemphero Amene Mulungu Amamva

28 Mdima Ukagwa Masana

32 “Ndifunika Kuti Ndidziŵe Bwino Nkhaniyi”

Kodi Ngozi Zapamsewu—Sizingakuchitikireni? 12

Dziŵani mmene mungapeŵere zinthu ziŵiri zazikulu zimene zimachititsa ngozi zoopsa zapamsewu.

Kodi Ndichititse Opaleshoni Kuti Ndikhale Wokongola? 16

Achinyamata ambirimbiri akufuna kuchititsa opaleshoni monga njira yodzikongoletsera. Kodi zimenezi si zoopsa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena