Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g04 9/8 tsamba 1-3
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2004
  • Nkhani Yofanana
  • Tsankho Likuchitika Padziko Lonse
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Kodi Muli Ndi Mtima Watsankho?
    Galamukani!—2020
  • Kodi Tsankho Lidzatha Liti?
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Mapeto a Tsankho
    Galamukani!—2004
Onani Zambiri
Galamukani!—2004
g04 9/8 tsamba 1-3

Zamkatimu

September 8, 2004

Kodi Tsankho Lidzatha?

Tsankho limagawanitsa anthu ndipo lafika mpaka poyambitsa nkhondo. Kodi tsankho lingathetsedwe bwanji kuti lisadzakhaleponso mpaka kalekale?

3 Mitundu Yosiyanasiyana ya Tsankho

6 Zimene Zimayambitsa Tsankho

8 Mapeto a Tsankho

12 Achinyamata Amene Sachita Manyazi Kulankhula za Chikhulupiriro Chawo

14 Chinthu Chabwino Kuposa Kutchuka

19 Vuto la Mabanja Opanda Atate Likukula

21 Atate Amene Ana Amafunikira

24 Mmene Mungakhalire Tate Wabwino

31 “Mudzaŵerenga Liti Zonsezi?”

32 “Landisintha Kwambiri”

Kodi Ndingatani Kuti Ndipewe Kugonana Ndisanaloŵe M’banja? 28

Kugonana anthu asanaloŵe m’banja kwabweretsa mavuto aakulu. Kodi achinyamata angatani kuti apeŵe kugonana asanaloŵe m’banja n’kudziteteza ku mavuto?

[Chithunzi patsamba 2]

Kudera lapakati pa chigawo cha Tamil Nadu, ku India

Ana a fuko lodetsedwa ali kusukulu ya m’mudzi mwawo

[Mawu a Chithunzi]

© Mark Henley/Panos Pictures

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena