Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 8/06 tsamba 27-31
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
  • Galamukani!—2006
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • KODI PALI KUFANANA KOTANI?
  • ZINACHITIKA LITI?
  • NDINE NDANI?
  • NDINE NDANI?
  • KUCHOKERA M’MAGAZINI INO
  • Zithunzi Zoti Ana Apeze
  • MAYANKHO A MAFUNSO A PA TSAMBA 31
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2007
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2006
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2007
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2007
Onani Zambiri
Galamukani!—2006
g 8/06 tsamba 27-31

Kodi Mungayankhe Bwanji?

KODI PALI KUFANANA KOTANI?

1. Pa zochitika zomwe zalembedwa m’munsimu, lembani mzere kuzungulira zochitika zokhazo zomwe zinachitikira Mose ndi Yesu.

Anaitanidwa kuti achoke ku Igupto

Anapulumuka osaphedwa ali mwana

Anatulutsa madzi m’thanthwe

Anasala kudya masiku 40

Anaukitsa akufa

Anapachikidwa pa mtengo

Yehova anataya thupi lake

◆ Kodi Mose anaima liti pambali pa Yesu m’masomphenya?

․․․․․

◆ Kodi winanso ndani anaonekera naye limodzi?

․․․․․

◼ Kambiranani: Kodi Yesu anali mneneri ngati Mose m’njira zina ziti?—Machitidwe 3:22.

ZINACHITIKA LITI?

Lembani mzere kulumikiza chochitika chilichonse ndi chaka chomwe chinachitikira.

1077 B.C.E. Cha m’ma 940 Cha m’ma 844 Kuchokera mu 778 Kuchokera mu 322

2. Yesaya 1:1

3. Yona 1:14-17

4. 1 Mafumu 17:2, 3

NDINE NDANI?

5. Mwana wanga wamkazi anapha abale ake n’kulanda ufumu wa Yuda. Koma mofanana ndi ine, anali mfumukazi yomwe inafa mochita kuphedwa.

NDINE NDANI?

6. Ndinaneneratu malo amene Mesiya anadzabadwirako.

KUCHOKERA M’MAGAZINI INO

Yankhani mafunso awa, ndipo lembani vesi kapena mavesi a m’Baibulo omwe akusowapo.

Tsamba 11 N’chifukwa chiyani Mulungu amaona kuti magazi ndi opatulika? (Genesis 9:․․․)

Tsamba 13 Kodi bwato losodzera nsomba ku Galileya m’zaka 100 zoyambirira linkatha kunyamula anthu angati? (Yohane 21:․․․)

Tsamba 24 Kodi chimachitika n’chiyani tikaika zosowa za ena patsogolo pa zosowa zathu? (Miyambo 11:․․․)

Tsamba 29 Kodi tikudziwa bwanji kuti anthu akufa sakukhala kumwamba ngati angelo? (Mlaliki 9:․․․)

Zithunzi Zoti Ana Apeze

Kodi mungathe kupeza zithunzi izi m’magazini ino? M’mawu anuanu, fotokozani zimene zikuchitika pa chithunzi chilichonse.

(Mayankho ali pa tsamba 27)

MAYANKHO A MAFUNSO A PA TSAMBA 31

1. Anaitanidwa kuti achoke ku Igupto. Anapulumuka osaphedwa ali mwana. Anasala kudya masiku 40. Yehova anataya thupi lake.

◆ M’masomphenya a kusandulika kwa Yesu.—Mateyu 17:1-3.

◆ Eliya.

2. Kuchokera mu 778 B.C.E.

3. Cha m’ma 844 B.C.E.

4. Cha m’ma 940 B.C.E.

5. Yezebeli.

6. Mika.—Mika 5:2.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena