Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 6/09 tsamba 1
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2009
  • Nkhani Yofanana
  • Kuchotsa Mimba Si njira yabwino
    Galamukani!—2009
  • Kutaya Mimba—Kodi Ndiko Yankho?
    Galamukani!—1995
  • Chidziŵitso pa Nyuzi
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Kodi Baibulo Limanena Zotani pa Nkhani Yochotsa Mimba?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
Onani Zambiri
Galamukani!—2009
g 6/09 tsamba 1

Zamkatimu

June 2009

Kodi Kuchotsa Mimba N’koipa Chifukwa Chiyani?

Kodi moyo wa munthu umayamba liti? Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene Baibulo limanena zomwe zikugwirizananso ndi sayansi.

3 Kuchotsa Mimba Si Njira Yabwino

5 Kodi Moyo wa Munthu Umayamba Liti?

6 Chifukwa Chake Sitinachotse Mimba

10 Kodi Pali Vuto Lililonse ndi Kukhalitsa Padzuwa?

12 Ndinamasulira Mabuku Mobisa kwa Zaka 30

16 Mzinda wa Plovdiv Ndi Wakale Kwambiri

19 Zimene Achinyamata Amadzifunsa

Kodi Ndingatani Kuti Ndizigwiritsa Ntchito Nthawi Moyenera?

28 Thandizani Ana Anu Kuti Akule Bwino

29 Zochitika Padzikoli

30 Wodwala Ali Ndi Ufulu Wosankha

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 Msonkhano Wachigawo wa Mboni za Yehova Wakuti: “Khalani Maso”

Kodi Muyenera Kuopa Anthu Akufa? 22

N’chifukwa chiyani anthu ambiri m’mayiko osiyanasiyana amaopa anthu akufa? Kodi n’chiyani chingathandize anthu kuthetsa mantha amenewa?

Achinyamata a Katolika Anauzidwa Kuti Azilalikira 24

Mwambo wa Tsiku la Achinyamata Padziko Lonse wa 2008, unachitikira ku Australia ndipo kunali anthu ambiri zedi. Anthu enanso okwana 500 miliyoni anaonera mwambowu pa TV. Kodi mwambowu unasonyeza chiyani za chikhulupiriro cha achinyamata?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena