Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 7/12 tsamba 2-3
  • Kodi Inuyo Mungakonde Kusintha Zinthu Ziti?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Inuyo Mungakonde Kusintha Zinthu Ziti?
  • Galamukani!—2012
  • Nkhani Yofanana
  • Tikufunikira Dziko Labwino
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2021
  • Kodi Zinthu Zopanda Chilungamo Zidzatha Padzikoli?
    Nkhani Zina
  • Kodi Tsankho Lidzatha Liti?
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Kodi N’chiyani Chikuyenera Kusintha?
    Galamukani!—2012
Onani Zambiri
Galamukani!—2012
g 7/12 tsamba 2-3

Kodi Inuyo Mungakonde Kusintha Zinthu Ziti?

Kodi ndi zinthu ziti padzikoli zimene zimakudetsani nkhawa kwambiri?

NJALA

UMPHAWI

MATENDA

KUPHWANYA MALAMULO

KUPANDA CHILUNGAMO

NKHONDO

KUWONONGEKA KWA MPWEYA, NTHAKA NDI MADZI

TSANKHO

Kodi pa zinthu zotsatirazi, ndi ziti zimene mumalakalaka zitachitika?

ANTHU AMITUNDU YONSE ATAMAKHALA MOGWIRIZANA

ALIYENSE ATAMAPEZA CHITHANDIZO CHAMANKHWALA MOSAVUTA

TSANKHO LITATHA

ALIYENSE ATAMAPEZA CHAKUDYA NDI MADZI AKUMWA OKWANIRA

ANTHU ATAMAKHALA M’NYUMBA ZAWO MOPANDA MANTHA

ANTHU ALI NDI MALO ABWINO OKHALA

ALIYENSE ATAMACHITIRIDWA ZINTHU MWACHILUNGAMO

Kodi mukuganiza kuti zimene mumalakalakazi zidzachitikadi? Ena amaganiza kuti zikhoza kuchitika ngati maboma atamayendetsa bwino zinthu. Koma kodi atsogoleri a mayiko angasinthedi zinthu padzikoli? Kodi zimene zikuchitika masiku ano zikusonyeza kuti iwo angasinthedi zinthu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena