Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 4/13 tsamba 16
  • Mukhoza Kulowa pa Webusaiti Yathu Mosavuta

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mukhoza Kulowa pa Webusaiti Yathu Mosavuta
  • Galamukani!—2013
  • Nkhani Yofanana
  • Vidiyo Yatsopano Yothandiza Poyambitsa Maphunziro a Baibulo
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Kodi Mumagwiritsa Ntchito Laibulale ya JW?
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Laibulale Yokwanira M’dzanja Limodzi
    Kodi Zopereka Zanu Zimagwiritsidwa Ntchito Bwanji?
  • Ana ndi Mafoni—Mbali Yoyamba: Kodi Mwana Wanga Akhale ndi Foni?
    Mfundo Zothandiza Mabanja
Onani Zambiri
Galamukani!—2013
g 4/13 tsamba 16

Mukhoza Kulowa pa Webusaiti Yathu Mosavuta

Kuyambira ndi Galamukani! ino ya mwezi wa April, magazini ya Galamukani! izikhala ndi kachidindo kotchedwa QR (quick response). Kachidindo kameneka kazikhala ndi manambala osaoneka omwe azithandiza munthu kulowa pa Webusaiti yathu mosavuta. Mungathe kugwiritsa ntchito njira imeneyi ngati muli ndi foni yapamwamba yokhala ndi kamera komanso Intaneti.

  1. Pangani dawunilodi pulogalamu yomwe imatha kuzindikira manambala a QR.

  2. Tsegulani pulogalamuyo.

  3. Jambulani kachidindo ka QR.

Nthawi yomweyo foni yanu itsegula Webusaiti yathu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena