Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 8/13 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2013
  • Nkhani Yofanana
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
Onani Zambiri
Galamukani!—2013
g 8/13 tsamba 1-2

Zamkatimu

August 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

NKHANI YA PACHIKUTO

Kodi N’zotheka Kukhala Ndi Moyo Wautali?

TSAMBA 6 MPAKA 9

3 Zochitika Padzikoli

4 Mfundo Zothandiza Mabanja

Mmene Mungathandizire Mwana Wanu Amene Amadzivulaza Mwadala

10 Kucheza ndi Anthu

Dokotala Woona za Mafupa Akufotokoza za Chikhulupiriro Chake

12 Zikhulupiriro

Kodi Muyenera Kukhulupirira Utatu?

14 Zimene Baibulo Limanena

Mowa

16 Kodi Zinangochitika Zokha?

Mbalame ya Albatross Yosatopa ndi Kuuluka

MUNGAPEZE ZAMBIRI PA WEBUSAITI YA

www.jw.org

ACHINYAMATA

ZIMENE ACHINYAMATA AMADZIFUNSA

N’Chifukwa Chiyani Ndimadzivulaza Mwadala?

Mtsikana wina, dzina lake Jerrine, ananena kuti: “Nthawi zonse ndinkati ndikadzicheka mwadala, ndinkasokonezeka maganizo ndipo ndinkaganiza kuti imeneyi ndi njira yabwino yothanirana ndi mavuto anga.” Vuto limeneli ndi lofala kwambiri kwa achinyamata. Koma n’chifukwa chiyani amadzivulaza? Kodi amachita zimenezi potengera anzawo? Kodi mungatani ngati inunso muli ndi vuto limeneli?

(Fufuzani pa mawu akuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ACHINYAMATA)

ANA

Werengani nkhani zomwe zafotokozedwa pogwiritsa ntchito zithunzi. Gwiritsani ntchito nkhanizi kuthandizira ana anu kudziwa zambiri za anthu otchulidwa m’Baibulo komanso kuwathandiza kuti akhale ndi makhalidwe abwino.

(Fufuzani pa mawu akuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ANA)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena