Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 12/13 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2013
  • Nkhani Yofanana
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
  • Zamkatimu
    Galamukani!—2013
Onani Zambiri
Galamukani!—2013
g 12/13 tsamba 1-2

Zamkatimu

December 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania.

NKHANI YA PACHIKUTO

Kodi Ofalitsa Nkhani Tingawakhulupirire?

TSAMBA 4 MPAKA 7

3 Zochitika Padzikoli

8 Anthu Ndi Mayiko

Dziko la Brazil

10 Zimene Baibulo Limanena

Yesu

12 Mfundo Zothandiza Mabanja

Kodi Mungatani Kuti Muzimvetsera Mwamuna Kapena Mkazi Wanu Akamalankhula?

14 Agulugufe Ochita Zinthu Mogometsa

15 Mlozera Nkhani wa Magazini a Galamukani! a 2013

16 Kodi Zinangochitika Zokha?

Kuchuluka kwa Zinthu Zimene DNA Imasunga

MUNGAPEZE ZAMBIRI PA WEBUSAITI YA

www.jw.org

ACHINYAMATA

Mukhoza kupeza mayankho ochokera m’Baibulo a mafunso ambiri amene achinyamata amadzifunsa. Nkhani zake ndi monga:

• “Kodi Ndingatani Ngati Anthu Ena Akukonda Kunena za Ine?”

• “Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani pa Nkhani Yotumizirana Mameseji ndi Zinthu Zina Zolaula?”

Werengani nkhanizi kuti mudziwe mmene Baibulo lingathandizire achinyamata kuthana ndi mavuto amene amakumana nawo.

(Fufuzani pa mawu akuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA >ACHINYAMATA)

ANA

Werengani nkhani zomwe zafotokozedwa pogwiritsa ntchito zithunzi. Gwiritsani ntchito nkhanizi kuthandiza ana anu kudziwa zambiri za anthu otchulidwa m’Baibulo komanso kuwathandiza kuti akhale ndi makhalidwe abwino.

(Fufuzani pa mawu akuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ANA)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena