Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g19 No. 2 tsamba 2
  • Mawu Oyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba
  • Galamukani!—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Zili M’magaziniyi
    Galamukani!—2019
  • Kalata Yochokera ku Bungwe Lolamulira
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Kodi Tingagwiritse Ntchito Bwanji Kabuku Kakuti Kodi Ndani Akuchita Chifuniro cha Yehova Masiku Ano?
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Mmene Mungaphunzitsire Ana Zinthu Zokhudza Mulungu—Kodi Njira Zabwino Ndi Ziti?
    Nsanja ya Olonda—2011
Onani Zambiri
Galamukani!—2019
g19 No. 2 tsamba 2

Mawu Oyamba

Makhalidwe 6 Amene Muyenera Kuphunzitsa Ana Anu

Kodi mumafuna kuti mwana wanu azidzadziwika ngati munthu wotani akadzakula?

  • Wodziletsa?

  • Wodzichepetsa?

  • Wopirira?

  • Wodalirika?

  • Woganiza bwino?

  • Wokhulupirika?

Ana sangakhale ndi makhalidwe amenewa paokha. Amafunika kuti inuyo makolo muwathandize.

Magaziniyi yafotokoza makhalidwe ofunika 6 omwe muyenera kuphunzitsa ana anu kuti adzakhale anthu odalirika.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena