Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g21 No. 1 tsamba 16
  • Kodi mukufuna kudziwa zambiri?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi mukufuna kudziwa zambiri?
  • Galamukani!—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Nzeru Yeniyeni Ikufuula
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • “Mtima Wodekha Ndiwo Moyo wa Munthu”
    Galamukani!—2020
  • Kodi Mumagwiritsa Ntchito “Nzeru Yochokera Kumwamba” pa Moyo Wanu?
    Yandikirani Yehova
  • ‘Wodala Munthu Wopeza Nzeru’
    Nsanja ya Olonda—2001
Onani Zambiri
Galamukani!—2021
g21 No. 1 tsamba 16

Kodi mukufuna kudziwa zambiri?

Pafoni pakuoneka imodzi mwa mavidiyo ophunzitsira Baibulo.

Munthu wina wanzeru analemba kuti: “Nzeru ndiyo chinthu chofunika kwambiri. Peza nzeru, ndipo pa zinthu zonse zimene upeze, upezenso luso lomvetsa zinthu.” (Miyambo 4:7) Mlengi wathu amatithandiza kuti tikhale ndi nzeru komanso kuti tizimvetsa bwino zinthu n’cholinga choti tizisankha zinthu mwanzeru n’kumakhala ndi moyo wosangalala.

Ngati mukufuna kudziwa zambiri zokhudza nzeru zothandiza zomwe zimapezeka m’Baibulo, pitani pa jw.org. Pamenepa mupezapo zinthu monga . . .

  • BAIBULO

  • MAVIDIYO

  • MAKATUNI

  • ZOCHITIKA PA MOYO WA ANTHU ENA

  • NKHANI

Zonsezi zikupezeka mwaulere ndipo ndi zothandiza kwa anthu a misinkhu yonse komanso ochokera kulikonse.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena