Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • le tsamba 4-5
  • Kodi Ndani Anakulengani?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Ndani Anakulengani?
  • Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
  • Nkhani Yofanana
  • Chigawo 3
    Mverani Mulungu
  • Kodi N’chifukwa Ninji Munthu Amafa?
    Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
  • Kodi Moyo Unali Wotani m’Paradaiso?
    Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha
  • Tingaphunzire ku Banja Loyamba la Anthu
    Nsanja ya Olonda—2000
Onani Zambiri
Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
le tsamba 4-5

Kodi Ndani Anakulengani?

1 Mulungu analenga kumwamba ndi dziko lapansi.—Genesis 1:1

2 Mulungu ali ndi dzina. Dzina lake ndilo Yehova.—Salmo 83:18

Yehova amakhala kumwamba. Iye ali mzimu. Simungamuone.—Yesaya 66:1; Yohane 1:18; 4:24

3 Yehova Mulungu anapanga angelo ambiri kumwamba. Iwo nawonso ali mizimu. Iwo onse anali abwino. Kale iwo nthaŵi zina anali kuvala matupi a anthu kotero kuti anthu awaone.—Ahebri 1:7

4 Yehova anapanga nyama kalekale, munthu asanapangidwe.—Genesis 1:25

5 Yehova anapanganso munthu wotchedwa Adamu ndi mkazi wake wotchedwa Hava.—Genesis 1:27

Mulungu anawaika m’munda wokongola, kapena paradaiso. Iye anapangira Adamu mkazi mmodzi yekha. Mwamunayo anayenera kukhala ndi mkazi wake mmodziyo.—Genesis 2:8, 21, 22, 24

6 Munthu ndiye moyo.—Genesis 2:7

7 Nyama zili miyoyo.—Genesis 1:24

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena