Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 18
  • Dalitsani Ubale Wathu Wachikristu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Dalitsani Ubale Wathu Wachikristu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Dzina la Atate Wathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tizichita Zinthu Zogwirizana Ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova
  • Ntchito Yomwe Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 18

Nyimbo 18

Dalitsani Ubale Wathu Wachikristu

(1 Petro 2:17)

1. Kristu mokomadi

Anaphunzitsatu,

Ophunzira ake

Napatsa mtendere.

Anasonyeza chikondi,

Cha chilungamocho,

Nasonyeza kudekha ndi

Chikondi chowona.

(Korasi)

2. Akristu akondwa

Omvera Yehova!

Ofatsa adala,

Omvera Mulungu!

Ophunzira a Yesuwo

Akonda ubale,

Amalengeza Ufumu

Pamodzi mokondwa.

(Korasi)

3. Timke ndi mbiriyo

Kwa onse ofuna,

Athandizenitu

Kusankha Mulungu.

Muwathandize kumfuna,

Adakapezeka,

Agwirizane Mu’bale,

Kuti akondwere.

(KORASI)

Titama inu Ya;

Mulidi wabwino.

O Atate wakumwamba,

M’dalitse ubale wathu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena