Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 35
  • Njira Yoposa ya Chikondi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Njira Yoposa ya Chikondi
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani Woleza Mtima
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Mulungu Ndiye Chikondi”
    Imbirani Yehova
  • “Mulungu Ndi Chikondi”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalani Ndi Chikondi Chimene Sichitha Konse
    Nsanja ya Olonda—2009
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 35

Nyimbo 35

Njira Yoposa ya Chikondi

(1 Akorinto 13)

1. Mulungu ndiye chikondi,

Yendani m’chikondicho,

Cha Mulungu ndi cha mnansi;

Chiri chanu muzonse.

Nkana chidziŵitso chonse,

Lirime ndi ulosi,

Ngati chikondi chisoŵa,

Tikanakhala chabe.

2. Ngakhale talalikira

Ndiponso kupilira;

Tidzapindula motani.

Tikasoŵa chiyero?

Chikondicho nchachifundo,

Sichichita choipa,

Chikondi sichidzikuza,

Sichimachita nsanje.

3. Chikondi sichipsa mtima,

Sichikonda choipa.

Chimapilira molimba,

Chimakonda zabwino.

Chikondi chipitiriza

Potumikira M’lungu;

Chotero njira yoposa

Ndinjira ya chikondi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena