Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 51
  • Kukondweretsa Mtima wa Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kukondweretsa Mtima wa Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tikondweretse Mtima wa Yehova
    Imbirani Yehova
  • Tizisangalatsa Mtima wa Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ana Amene Amakondwereta Mtima wa Yehova
    Nsanja ya Olonda—1987
  • Kodi Mumamva Bwanji?
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 51

Nyimbo 51

Kukondweretsa Mtima wa Yehova

(Miyambo 27:11)

1. Mulungu, ife tasankha;

Kuchita chifuno chanu.

Tidzakhala ndi mbalitu

Yokondweretsa mtimanu.

2. Tisabwevuke kwa inu;

Woyesayo ndiwabodza.

Masiku onse tikondwe

Ndi malamulo anuwo.

3. Kapolo wanu wanzeru,

Athandiza ife tonse,

Atidyetsa m’nthaŵi yake,

Tichite chifuno chanu.

4. Mutipatse mzimu wanu,

Tikhale odalirika

Kubweretsa chitamando,

Kukondweretsa mtimanu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena