Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 162
  • Zosowa Zanga Zauzimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zosowa Zanga Zauzimu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Phunziro 3
    Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Kukonzekera Kupita Kolalikira
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • “Ndine Pano! Munditumize Ine”
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 162

NYIMBO 162

Zosowa Zanga Zauzimu

Losindikizidwa

(Mateyu 5:3)

  1. 1. Tonsefe tilitu ndi

    Zosowa za uzimu.

    Timafuna kudziwatu

    Mulungu woona.

    Anthu amafufuza,

    Mayankho alipotu.

    M’mawu ake, M’Baibulo.

    Tiziwawerenga.

    (KOLASI)

    Ine ndimutamanda.

    Ndizimvera mawu ake.

    Ndipo ndim’tumikira.

    Andisamalira.

    Ndipitiliza

    Kukhala mnzake.

  2. 2. Ndizipezabe nthawi

    Yowerenga mawuwo,

    N’kumapeza zinthu zomwe

    Ndingamasinthebe.

    Ena safuna kumva.

    Ndiziwapempherera

    Kuti nawo amudziwe,

    N’kumuyandikira.

    (KOLASI)

    Ine ndimutamanda.

    Ndizimvera mawu ake.

    Ndipo ndim’tumikira.

    Andisamalira.

    Ndipitiliza

    Kukhala mnzake.

    Ine ndimutamanda.

    Ndizimvera mawu ake.

    Ndipo ndim’tumikira.

    Andisamalira.

    Ndipitiliza

    Kukhala mnzake.

    Ine ndimutamanda.

    Ndizimvera mawu ake.

    Ndipo ndim’tumikira.

    Andisamalira.

    Ndipitiliza

    Kukhala mnzake.

(Onaninso Mat. 5:6; 16:24; Yes. 40:8; Sal. 1:1, 2; 112:1; 119:97; 2 Tim. 4:4.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena