Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 161
  • “Ndimasangalala Kuchita Zimene Mumafuna”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ndimasangalala Kuchita Zimene Mumafuna”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Chimwemwe Chosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tili Ndi Zifukwa Zambiri Zokhalira Osangalala
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—2000
  • Tili ndi Zifukwa Zambiri Zokhalira Osangalala
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 161

NYIMBO 161

“Ndimasangalala Kuchita Zimene Mumafuna”

Losindikizidwa

(Salimo 40:8)

  1. 1. Yesu atangobatizidwa

    Munamulimbikitsatu.

    Ankafunitsitsa kuchita

    Zimene mumafuna.

    Sanagonje mu mayesero.

    Anadziperekadi.

    Anayeretsa dzina lanu,

    Nane ndimutsanzire.

    (KOLASI)

    Kuchita zofuna zanu

    Kumandisangalatsadi.

    N’kamamvera mawu anu,

    Ndidzasangalalabe.

    Kuchita zofuna zanu

    Kumandisangalatsadi.

    Ndimadziwa m’mandikonda.

    Ndizichitabe zomwe

    Mumafuna.

  2. 2. Kudziwa za inu Yehova

    Kumandipatsa chimwemwe.

    Ndizilalikira za inu

    Monga mboni yanudi.

    Kutumikira ndi abale

    Kumandisangalatsa.

    Ndimanyadira podziwika

    Ndi dzina lanu M’lungu.

    (KOLASI)

    Kuchita zofuna zanu

    Kumandisangalatsadi.

    N’kamamvera mawu anu,

    Ndidzasangalalabe.

    Kuchita zofuna zanu

    Kumandisangalatsadi.

    Ndimadziwa m’mandikonda.

    Ndizichitabe zomwe

    Mumafuna.

    Zomwe mumafuna.

(Onaninso Sal. 40:3, 10.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena