Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 69
  • Kudzipatulira Kwaumulungu ndi Chikhutiro

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kudzipatulira Kwaumulungu ndi Chikhutiro
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Onjezerani Kudzipereka kwa Mulungu pa Chipiriro Chanu
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Tikulandirani ku Misonkhano Yachigawo ya “Kudzipereka Kwaumulungu”
    Nsanja ya Olonda—1989
  • Wonjezerani Pachipiriro Chanu Kudzipereka Kwaumulungu
    Nsanja ya Olonda—1993
  • Kodi Munthu Angakhaledi Wokhutira ndi Zimene ali Nazo?
    Nsanja ya Olonda—2010
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 69

Nyimbo 69

Kudzipatulira Kwaumulungu ndi Chikhutiro

(1 Timoteo 6:6)

1. Kuti tidalitsidwe,

Tikhale okhutira,

Timveretu Mawu a Ya

Ndi umulungu wathu.

Kupembedza ndi kwa phindu,

Kupeŵetsadi machimo.

Tsiku n’tsiku M’njira ya Ya,

Kumachititsa changu.

2. Kukhutira n’za M’lungu,

Tipanga chosankhachi:

M’gwadireni, Dziŵitsani,

Wonani Ufumuwo.

Tilandira chiitano

Tiyende m’chipulumutso.

Mwachimwemwe Tiganiza

Kulipsira kwa M’lungu.

3. Tithokoza Mulungu,

Ngakhale tidedwatu,

Adalitsa Mapembedzo

Munthaŵi zovutazi.

Tisamalire cho’nadi,

Tichotsetu mantha onse.

Tikhaletu Okhutira

Ndi kudziŵa Chikristu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena