Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 97
  • Mikhalidwe ya Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mikhalidwe ya Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Makhalidwe a Yehova
    Imbirani Yehova
  • Makhalidwe a Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Ndi Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Ndiye Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 97

Nyimbo 97

Mikhalidwe ya Yehova

(Chivumbulutso 4:11)

1. M’lungu wokuzika mumphamvu,

Kasupe wa kuunika,

Chilengedwe chimanena;

Zambiri pa Armagedo.

2. Zimene mwapanga nzanzeru!

Ziti mwazipanga bwino.

Mawu anu timawona

Nzeru yanu yoŵalayo.

3. Mpando wanu ndiwolungama.

Mwadziŵitsa chilungamo.

Mutipatse khutu lomva,

Kuti tiwopetu inu.

4. Tinyadira m’chikondi chanu;

Tiri nachotu mangaŵa.

Tidzabukitsa mokondwa,

Mikhalidwe ya inuyo!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena