Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 118
  • Kuchirikiza Nyumba ya Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuchirikiza Nyumba ya Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 118

Nyimbo 118

Kuchirikiza Nyumba ya Mulungu

(Malaki 3:10)

1. A m’nyumba ya M’lungu tisonyeze

Kusanyalanyaza malo ake,

Za nyumba yolingaliridwayo

Kuti dzina lake lidzakhale.

Monga Nehemiya mosamala

Anabwezeretsa kulambira

Nafenso titero ndi ‘chachikhumi,’

Motero tisonyeza kumukonda.

(Korasi)

2. Banja la M’lungu ndi laumodzi,

Nyumba imene asamalira.

Kapolo wake amtumikira,

Chotero achititsa mtendere.

Tidze kwa M’lungu ndi ‘chuma’ chathu;

Zopereka zidzetsa ulemu.

Adalitsa bwino abanja lake,

Motero timtumikire mokondwa.

(KORASI)

Tichirikize nyumbayo.

‘Idzani mulambiremo.’

Nyumba yake ndiyo banja;

Adzakhalamotu kosatha.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena