Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 4
  • Athandizeni Kukhala Olimba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Athandizeni Kukhala Olimba
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 4

Nyimbo 139

Athandizeni Kukhala Olimba

(Mateyu 28:19, 20)

  1. Kuphunzitsa nkhosa za M’lungu

    Ndi mwayi wapadera.

    Yehova wawatsogolera.

    Amakonda cho’nadi.

    (KOLASI)

    Yehovatu tikupempha

    Kuti muziwateteza.

    Mwa Yesu tikupemphani: Athandizenibe

    Akhale olimba.

  2. Mayesero akawagwera,

    Timawapempherera.

    Tayesetsa kuwaphunzitsa,

    Ndipo adalitsidwa.

    (KOLASI)

    Yehovatu tikupempha

    Kuti muziwateteza.

    Mwa Yesu tikupemphani: Athandizenibe

    Akhale olimba.

  3. Akhale okudalirani,

    Inu M’lungu ndi Yesu

    Apirire pamayesero,

    Akalandire moyo.

    (KOLASI)

    Yehovatu tikupempha

    Kuti muziwateteza.

    Mwa Yesu tikupemphani: Athandizenibe

    Akhale olimba.

(Onaninso Luka 6:48; Mac. 5:42; Afil. 4:1.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena