Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 119
  • Kugwiritsitsa “Chiyembekezo Chachimwemwe”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kugwiritsitsa “Chiyembekezo Chachimwemwe”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu
    Imbirani Yehova
  • Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 119

Nyimbo 119

Kugwiritsitsa “Chiyembekezo Chachimwemwe”

(Tito 2:13, NW)

1. Anthu afufuza mumdima kwazaka.

Izi nzachabe zosautsa mtima.

Kuipa tsopano kwachulukadi;

Mapeto omvetsa chisoni.

(Korasi)

2. Tikondwa kudziŵa chifukwa chimene

Mulungu walolera kuipako.

Kudzathetsedwa ndi Kristu Yesuyo.

Ambali yake adzaimba.

(Korasi)

3. Mutsiku lathu chilengezo chimveka.

Anthu sadzafunikira kuwopa.

‘M’lungu adzamasula chilengedwe.’

Tonse tiyang’ane mtsogolo.

(KORASi)

Kondwerani, Ufumuwo wadza.

Mwana wake azadzetsa ufulu.

Masoka a anthu adzachoka.

Tigwiritsitse chiyembekezochi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena